26/11/2024
Ena amkafusa kuti kodi bungwe la ADRA limapanga chiyani , nanga eni wake ndindani ?
Yankho bungwe limeneli ndi la katolika ,koma linapatsidwa kumpingo wa SDA ,pouthokoza mpingowu kuti unakwanilitsa popanga nawo mgwilizano ndi papa Ku Vatican ,
Bungwe limeneli amene amalithandiza ndi papa ,bungweli limalimbikitsa kukonza makondomu ,ndikumalimbikitsaso anthu awo akhilisitu awo kugwilitsa ntchito makondomuwa ,
Mwa ichi mafuso mkumati kodi makondomu ndi ofunikila kwa mkhilisitu ?
Mu zeni zeni ayi ndithu uku ndikulimbikitsa kuti anthu adzikonda kupanga chigololo ,zomwe ndi Mulungu ndi kutali kwambili ,
Komatu mumpingomu malamulo alipo ndithu akuti usachiche chigololo koma zimawonetsa kuti zimangolankhulidwa koma osachita ,zomwe zimawonetsela kuti ,
Kayimidwe ka mpingo wa SDA ndikakugwa ndithu chifukwa ndizosatheka mpingo kumalimbikitsa za makondomu ayi ,
Zachisoni zina mzakuti ndale ,ndi chikhilisitu ndi zinthu ziwili zosiyana ,koma zomwe zili apa mzakuti wamkulu wa bungwe ili ndi manganya amene ali wachiwili kwa pulezident wadziko lino ,
Ndiye izi zowopsya kwambili ena timadabwa kuti ndichifukwa chiyani Mtsogoleli wa mpingo wa SDA kuno Ku Malawi bwanji amakondana ndi chakwela pulezident wadziko lino?
Yankho mlakuti kuseliko adagwilizana koma anthu amawabisila ,izi mzofunika kwa munthu amene ali ndi ganizo lofuna kupulumuka akuyenela kutsekulapo maso ake ,ndikuchitapo kanthu ,
Kodi khisitu ndi Beliyali agwilizana bwanji ????